Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/10 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 12/10 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

N’zosangalatsa kwambiri kuona mmene Yehova akudalitsira ntchito yathu muno m’Malawi. Tsopano tili ndi mipingo 1,235 ndiponso timagulu takutali tokwana 19. Ndipo mu March, mwezi womwe tinali ndi Chikumbutso, ofalitsa ambiri anawonjezera nthawi imene amathera mu utumiki wakumunda. Chifukwa cha zimenezi tinathera maola okwana 1,208,954 polalikira uthenga wabwino wa Ufumu ndiponso kupanga ophunzira atsopano. Tinagawira magazini okwana 424,461 komanso kuchititsa maphunziro a Baibulo okwana 82,797. Kuwonjezera pa zimenezi, tamaliza kumanga Nyumba za Ufumu zoposa 1,000 m’gawo la nthambi yathu ndipo nyumba zimenezi zikugwiritsidwa ntchito pa kulambira koyera.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena