Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/11 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 10

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 10
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 10
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 1/11 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa January 10

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 10

Nyimbo Na. 50 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 1, ndime 1-7 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Mbiri 33-36 (Mph. 10)

Na. 1: 2 Mbiri 34:12-21 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Tingaphunzire Chiyani kwa Mariya, Mayi a Yesu? (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Yesu Anali Chabe Mtsogoleri Wachipembedzo?—rs tsa. 424 ndime 3 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 25

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 15: Muzilankhula Mwaubwenzi Polalikira. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki tsamba 118, ndime 1, mpaka tsamba 119, ndime 5.

Mph. 15: “Ntchito Yosangalatsa Kwambiri.” Mafunso ndi mayankho. Mwachidule funsani wofalitsa kuti afotokoze chimwemwe chimene wapeza pokhala ndi phunziro la Baibulo lopita patsogolo.

Nyimbo Na. 28 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena