Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/11 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 17

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 17
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 17
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 1/11 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa January 17

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 17

Nyimbo Na. 35 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 1 ndime 8-15 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Ezara 1-5 (Mph. 10)

Na. 1: Ezara 3:1-9 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Ayuda Ambiri Sanavomereze Kuti Yesu Ndi Mesiya?—rs tsa. 425 ndime 1 ndi 2 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Mzimu umabwerera Motani kwa Mulungu?—Mlal. 12:7 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 43

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kufunika Kobwereza Mfundo Mu Utumiki Wakumunda. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki tsamba 206 mpaka 207. Chitani chitsanzo chachidule chosonyeza mmene tingagwiritsire ntchito mfundo imodzi kapena ziwiri za m’nkhaniyi.

Mph. 20: “Kodi Mukudziwa Zimene Mungasankhe?” Mafunso ndi mayankho. Pofotokoza mawu oyamba, gwiritsani ntchito ndime 1 ndipo m’mawu anu omaliza tchulani mfundo za mu ndime 3. Nkhani yokambidwa ndi mkulu.

Nyimbo Na. 7 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena