Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/11 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 31

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 31
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 31
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 1/11 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa January 31

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 31

Nyimbo Na. 30 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 2 ndime 1-8 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Nehemiya 1-4 (Mph. 10)

Na. 1: Nehemiya 2:11-20 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Lemba la Yohane 1:1 Limatsimikizira Kuti Yesu ndi Mulungu?—rs tsa. 426 ndime 4 mpaka tsa. 427 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Zimene Tingachite Potsatira Mawu a Yesu a pa Mateyu 22:21 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 52

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 20: “Mphatso Yothandiza Kwa Mabanja.”—Gawo 2. (Ndime 7-13) Mafunso ndi mayankho. Pemphani omvera kufotokoza mmene mabanja awo apindulira pogwiritsa ntchito mfundo zina zomwe zili pa tsamba 6.

Mph. 10: “Phunzitsani Ana Anu Kuti Adzakhale Atumiki.” Mafunso ndi mayankho. Pemphani omvera kuti afotokoze njira zimene makolo awo anawathandizira kuti akhale ndi zolinga mu utumiki komanso kuyesetsa kuzikwaniritsa.

Nyimbo Na. 41 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena