Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/11 tsamba 8
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 1/11 tsamba 8

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

M’chaka cha 2010, m’Malawi muno munachitika Misonkhano Yachigawo yokwana 63. Misonkhanoyi inachitika mu Chichewa, Chitumbuka, Chiyao, Chitonga, Chingelezi ndi Chinenero Chamanja cha ku America. Chiwerengero cha anthu amene anapezeka pa misonkhano yonseyi ndi 225,855 ndipo anthu okwana 2,434 anabatizidwa m’madzi posonyeza kuti anadzipereka kwa Yehova. Zoonadi, galeta lakumwamba la Yehova likuyenda mwamphamvu pokwanitsa cholinga chake.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena