Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 4/11 tsamba 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa April 25

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa April 25
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 25
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 4/11 tsamba 7

Ndandanda ya Mlungu wa April 25

MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 25

Nyimbo Na. 14 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 6 ndime 1-9 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yobu 33-37 (Mph. 10)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (Mph. 20)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 20

Mph. 5: Zilengezo. “Agwiritseni Ntchito, Osati Kungowasunga.” Nkhani. Uzani omvera za mabuku alionse akale amene aunjikana pa mpingopo.

Mph. 10: “Lipoti la Chaka Chautumiki cha 2010.” Nkhani yokambirana yochokera pa Lipoti la Chaka Chautumiki cha 2010. Fotokozani mbali zimene zinapita patsogolo kwambiri pa ntchito yathu yolalikira padziko lonse m’chaka chautumiki chapitachi.

Mph. 20: “Kulambira kwa Pabanja N’kofunika Kwambiri Kuti Tidzapulumuke.” Nkhani yokambirana yochokera mu Nsanja ya Olonda ya October 15, 2009, tsamba 29-31. Funsani abale awiri omwe ndi mitu ya mabanja. Abalewo akhale amene amachititsa Kulambira kwa Pabanja nthawi zonse m’mabanja mwawo. Afotokoze mmene mabanja awo apindulira chifukwa chochita Kulambira kwa Pabanja nthawi zonse.

Nyimbo Na. 32 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena