Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/11 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 27

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 27
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 27
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 6/11 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa June 27

MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 27

Nyimbo Na. 44 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 9 ndime 1-9 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Masalimo 52–59 (Mph. 10)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (Mph. 20)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 27

Mph. 10: Zilengezo. “Kodi Ndiziwerengera Bwanji Nthawi Ndikakhala mu Utumiki?” Nkhani yokambidwa ndi mkulu. Mukamaliza kukamba nkhaniyi, chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingayambitsire phunziro la Baibulo Loweruka lolambirira m’mwezi wa July, pogwiritsa ntchito chitsanzo cha ulaliki patsamba 4. Limbikitsani onse kuti ayesetse kuyambitsa maphunziro.

Mph. 10: Konzekerani Kugawira Magazini M’mwezi wa July. Nkhani yokambirana. Kwa mphindi imodzi kapena ziwiri, tchulani nkhani zina zimene zili m’magaziniwo. Kenako sankhani nkhani ziwiri kapena zitatu, ndipo funsani omvera kuti anene mafunso ndi malemba amene tingagwiritse ntchito pogawira magaziniwo. Chitani zitsanzo zosonyeza zimene tinganene pogawira magazini iliyonse.

Mph. 15: Khalani Osamala Polalikira. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 197 mpaka 199. Chitani chitsanzo chosonyeza wofalitsa akuyankha mosasamala zimene anthu otsutsa amakonda kutinena kwanuko. Kenako chitani chitsanzo china chosonyeza wofalitsa akuyankha nkhani yomweyo mosamala.

Nyimbo Na. 47 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena