Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/12 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 30

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 30
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 30
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 1/12 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa January 30

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 30

Nyimbo Na. 47 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 1 ndime 10-15 ndi tchati patsamba 12 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yesaya 43-46 (Mph. 10)

Na. 1: Yesaya 45:15-25 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Kuleza Mtima Kwa Mulungu Kungatithandize Bwanji Kuti Tidzapulumuke?—2 Pet. 3:9, 15 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi N’zofunikadi Kutsatira Malamulo a Boma Okhudza Kumangitsa Ukwati?—rs tsa. 383 ndime 1-3 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 87

Mph. 5: Zilengezo. Pogwiritsa ntchito chitsanzo cha ulaliki chimene chili patsamba 4, chitani chitsanzo chosonyeza mmene mungayambitsire phunziro pa Loweruka loyambirira m’mwezi wa February.

Mph. 10: Kodi Ndiyenera Kudziwa Zotani Zokhudza Malo Ochezera a pa Intaneti?—Gawo 1. Nkhani yochokera mu Galamukani! ya July 2011, masamba 24 mpaka 27 ndi Galamukani! ya February 2012, tsamba 6 ndi 7.

Mph. 20: “Kodi Mwakonzekera Ngati Mutachita Ngozi?” Mafunso ndi mayankho. Gwiritsani ntchito mfundo za m’ndime yoyamba ndi yomaliza monga mawu oyamba ndi omaliza.

Nyimbo Na. 116 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena