Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/12 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 1/12 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

M’chaka chapitachi cha 2011, m’Malawi muno munachitika misonkhano yachigawo yokwana 69 ndipo anthu 243,470 anapezeka pa misonkhano imeneyi. Komanso pa misonkhano imeneyi anthu okwana 2,588 anasonyeza kudzipereka kwawo kwa Yehova mwa kubatizidwa. Zimenezi zikusonyeza kuti pali anthu ambiri amene akufunikira thandizo lathu kuti apite patsogolo mwauzimu.—Mat. 28:19-20.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena