Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/12 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 20

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 20
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 20
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 2/12 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa February 20

MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 20

Nyimbo Na. 44 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 2 ndime 8-15 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yesaya 58-62 (Mph. 10)

Na. 1: Yesaya 61:1-11 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Kudzipereka Kwathu kwa Mulungu Chili Chizindikiro Choti Timamukonda Ndiponso Kumukhulupirira? (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Mulungu Amakuona Bwanji Kupatukana?​—rs tsa. 385 ndime 4 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 87

Mph. 10: Zilengezo. Tchulani buku logawira m’mwezi wa March ndipo chitani chitsanzo chimodzi chosonyeza mmene tingagawirire bukulo.

Mph. 10: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Salimo 63:3-8 ndi Maliko 1:32-39. Kambiranani mmene mavesi amenewa angatithandizire mu utumiki.

Mph. 15: “Ntchito Yapadera Yoitanira Anthu ku Chikumbutso Idzayamba pa March 17.” Mafunso ndi mayankho. Gawirani kapepala kamodzi koitanira ku Chikumbutso kwa aliyense, kenako mukambirane zimene zili m’kapepalako. Mukamakambirana ndime 2, chitani chitsanzo chachidule chosonyeza mmene mungagawirire kapepalaka. Mukamakambirana ndime 3, pemphani woyang’anira utumiki kuti afotokoze zimene zakonzedwa kuti mugawire timapepalati m’gawo la mpingo wanu.

Nyimbo Na. 8 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena