Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/12 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 2/12 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Tikuyamikira abale ndi alongo amene akuchita upainiya wapadera mwakhama kwambiri kuti apititse patsogolo ntchito yotuta m’gawo la nthambi yathu. Mwachitsanzo, kwa nthawi yaitali, mpingo wa Chitimba umene uli kumpoto kwa dziko la Malawi lino wakhala uli ndi ofalitsa asanu okha. Koma chifukwa chothandizidwa ndi apainiya apadera, tsopano mu mpingowu muli ofalitsa 27. Chimenechi ndi chitsanzo chabwino kwambiri kwa tonsefe cha kudzipereka kwa abale ndi alongo amene akuchita upainiya wapadera.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena