Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/12 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 12

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 12
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 12
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 3/12 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa March 12

MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 12

Nyimbo Na. 99 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 3 ndime 4-11 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yeremiya 5-7 (Mph. 10)

Na. 1: Yeremiya 5:15-25 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Kale Mulungu Ankalola Munthu Kukwatirana ndi Mlongo Wake?—rs tsa. 387 ndime 2-3 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Yehova Amateteza Bwanji Anthu Ake Mwauzimu? (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 63

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kulitsani Luso la Kuphunzitsa—Gawo 2. Nkhani yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 57 ndime 3 mpaka pa kamutu ka patsamba 59.

Mph. 10: Lipoti la Chaka Chautumiki cha 2011. Nkhani yokambirana yochokera pa Lipoti la Chaka Chautumiki cha 2011 limene lili patsamba 3 mpaka 6. Fotokozani mbali zimene zinapita patsogolo kwambiri pa ntchito yathu yolalikira padziko lonse m’chaka chautumiki chapitachi.

Mph. 10: “Muzichita Zimenezi.” Mafunso ndi mayankho. Dziwitsani mpingo za malo ndi nthawi yochitira Chikumbutso.

Nyimbo Na. 109 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena