Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/12 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 28

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 28
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MAY 28
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 5/12 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa May 28

MLUNGU WOYAMBIRA MAY 28

Nyimbo Na. 98 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 6 ndime 17-24 ndi bokosi patsamba 48 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yeremiya 49-50 (Mph. 10)

Na. 1: Yeremiya 49:28-39 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi N’chifukwa Chiyani Dzina la Yehova Lili “Nsanja Yolimba”?—Miy. 18:10 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Mariya Anapita Kumwamba ndi Thupi Lake Lenileni?—rs tsa. 258 ndime 2-3 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 68

Mph. 10: Zilengezo. Pogwiritsa ntchito chitsanzo cha ulaliki chimene chili patsamba 4, chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingayambitsire phunziro la Baibulo Loweruka loyambirira m’mwezi wa June.

Mph. 25: “Inu Achinyamata, Khalani Ndi Mtima Wofuna Kutumikira Yehova.” Nkhani yokambirana. Funsani achinyamata awiri amene akuchita upainiya wothandiza kapena wokhazikika. Kodi n’chiyani chimene chinawathandiza kuti ayambe upainiya? Apindula chiyani chifukwa chochita upainiya? Ngati mumpingo wanu mulibe apainiya achinyamata, funsani atumiki othandiza awiri achinyamata. Kodi anali ndi maganizo otani asanakhale atumiki omwe anali olakwika? N’chiyani chimene chinawathandiza kuti ayenerere kukhala atumiki othandiza? Tsindikani kuti achinyamata onse ayenera kutumikira Yehova akadali ana.

Nyimbo Na. 45 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena