Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/12 tsamba 8
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 2
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JULY 2
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 6/12 tsamba 8

Ndandanda ya Mlungu wa July 2

MLUNGU WOYAMBIRA JULY 2

Nyimbo Na. 54 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 8 ndime 8-16 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Ezekieli 6-10 (Mph. 10)

Na. 1: Ezekieli 7:14-27 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Yonatani Ali Chitsanzo Chabwino Kwambiri pa Nkhani ya Kudzichepetsa?—1 Sam. 23:16-18 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi N’zoona Kuti Mkate ndi Vinyo Zimasandulika Kukhala Thupi ndi Magazi a Khristu?—rs tsa. 280 ndime 2–tsa. 282 ndime 1 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 64

Mph. 3: Zilengezo.

Mph. 8: Kukambirana Ndi Anthu mu Utumiki—Mbali Yoyamba. Kukambirana ndi omvera mfundo zimene zikupezeka m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 251 mpaka tsamba 253, ndime 1. Chitani chitsanzo chachidule chosonyeza mmene tingagwiritsire ntchito mfundo imodzi kapena ziwiri za m’nkhaniyi.

Mph. 24: “Misonkhano Yathu Yachigawo Imafotokoza Mfundo za Choonadi.” Mafunso ndi mayankho. Kambiranani “Zofunika Kukumbukira pa Msonkhano Wachigawo.” Mukamakambirana ndime 8, funsani woyang’anira utumiki kuti afotokoze zimene zakonzedwa pa ntchito yogawira timapepala toitanira anthu kumsonkhano wachigawo.

Nyimbo Na. 119 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena