Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/12 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 22

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 22
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 22
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 10/12 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa October 22

MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 22

Nyimbo Na. 43 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 14 ndime 1-5 ndi bokosi patsamba 112 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Hoseya 1-7 (Mph. 10)

Na. 1: Hoseya 6:1-10 ndi 7:1-7 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Mbali ya Padziko Lapansi ya Gulu la Yehova Tingaidziwe Bwanji?—rs tsa. 143 ndime 1-7 (Mph. 5)

Na. 3: Tsanzirani Yesu Ndipo Musamaope Kuchita Manyazi—Aheb. 12:2 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 130

Mph. 30: Zimene Achinyamata Amadzifunsa​—Kodi Ndingapeze Bwanji Anzanga Enieni? Mafunso ndi mayankho. Nkhani yochokera mu Galamukani! ya March 2009, tsamba 18 mpaka 20. Gwiritsani ntchito mfundo za m’ndime yoyamba ndi yomaliza monga mawu oyamba ndi omaliza. Ngati nthawi ilipo, werengani ndi kukambirana malemba amene ali m’nkhaniyi.

Nyimbo Na. 89 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena