Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/12 tsamba 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 31

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 31
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 31
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 12/12 tsamba 7

Ndandanda ya Mlungu wa December 31

MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 31

Nyimbo Na. 37 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 17 ndime 1-7 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Malaki 1-4 (Mph. 10)

Kubwereza za M’sukulu ya Utumiki wa Mulungu (Mph. 20)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 72

Mph. 10: “Nkhani Zatsopano Zimene Zizipezeka mu Nsanja ya Olonda.” Nkhani. Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulaliki chimene chili patsamba 8 posonyeza mmene tingagwiritsire ntchito magazini kuyambitsira phunziro la Baibulo pa Loweruka loyambirira la mwezi wa January.

Mph. 10: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Luka 10:38-42. Kambiranani mmene nkhani imeneyi ingatithandizire mu utumiki wathu.

Mph. 10: Mabuku Ogawira mu January ndi February. Nkhani yokambirana. Tchulani mfundo zachidule zimene zili m’bukulo kenako muchite zitsanzo ziwiri zosonyeza mmene tingagawirire bukulo.

Nyimbo Na. 134 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena