Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/13 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 11

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 11
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 11
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 3/13 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa March 11

MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 11

Nyimbo Na. 125 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 20 ndime 1-7 ndi bokosi patsamba 156 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu

Kuwerenga Baibulo: Maliko 13-16 (Mph. 10)

Na. 1: Maliko 14:22-42 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kukumbukira Imfa ya Yesu?​—rs tsa. 70 ndime 3-tsa. 71 ndime 2 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Zizindikiro za pa Chikumbutso Zimaimira Chiyani?​—rs tsa. 71 ndime 2-tsa. 72 ndime 2 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 109

Mph. 10: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Mateyu 10:7-10 ndi Luka 10:1-4. Kambiranani mmene mavesi amenewa angatithandizire mu utumiki.

Mph. 10: Njira Zowonjezera Utumiki Wanu​—Mbali Yoyamba. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Gulu, tsamba 111, ndime yoyamba mpaka tsamba 112 ndime yachiwiri. Funsani wofalitsa mmodzi kapena awiri amene asamukira mumpingo wachinenero china kapena amene aphunzira chinenero china kuti awonjezere utumiki wawo. Kodi ndi mavuto ati amene anali nawo ndipo anawatheta bwanji? Kodi achibale awo kapena mpingo unawathandiza bwanji? Kodi ndi madalitso otani amene apeza?

Mph. 10: “Khalani ndi Mtima Wosangalala Pokonzekera Chikumbutso.” Mafunso ndi mayankho. Kambiranani zimene mpingo wakonza zokhudza Chikumbutso. Fotokozani mmene ntchito yoitanira anthu ku Chikumbutso ikuyendera pa mpingo wanu.

Nyimbo Na. 8 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena