Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/13 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 20

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 20
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MAY 20
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 5/13 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa May 20

MLUNGU WOYAMBIRA MAY 20

Nyimbo Na. 78 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 23 ndime 9-15 ndi mabokosi patsamba 184 ndi 186 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yohane 8-11 (Mph. 10)

Na. 1: Yohane 8:12-30 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Tingatani Kuti Tisanyengedwe Ndi Anthu Ophunzitsa Zonama?—Aroma 16:17; 2 Yoh. 9-11 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi N’chifukwa Chiyani Mulungu Sanangolamula Kuti Onse Amene Azimumvera Adzakhala ndi Moyo Kosatha?—rs tsa. 123 ndime 2–tsa. 124 ndime 1 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 96

Mph. 10: Njira Zowonjezera Utumiki Wanu—Mbali Yachitatu. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Gulu, tsamba 116, ndime 1 mpaka tsamba 117 ndime 1. Funsani wofalitsa mmodzi kapena awiri amene anagwirapo ntchito yomanga Nyumba za Ufumu ngati alipo. Kodi n’chiyani chinawasangalatsa pochita utumikiwu?

Mph. 10: Yehova Amatithandiza Kukwaniritsa Utumiki Wathu. (Eks. 4:10-12; Afil. 4:13) Nkhani yokambirana yochokera m’Buku Lapachaka, tsamba 102, ndime 1 ndiponso tsamba 112, ndime 1 mpaka 3. Pemphani abale ndi alongo kuti afotokoze zimene aphunzirapo pa nkhanizi.

Mph. 10: “Kodi Ndi Ndani Amene Angakonde Magazini Awa?” Mafunso ndi mayankho. Pemphani abale ndi alongo kuti atchule anthu ogwira ntchito zina kapena anthu ogwira ntchito m’boma omwe ali m’gawo lawo amene angapindule ndi nkhani inayake imene ili m’magazini athu.

Nyimbo Na. 92 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena