Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/13 tsamba 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 29

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 29
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JULY 29
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 7/13 tsamba 7

Ndandanda ya Mlungu wa July 29

MLUNGU WOYAMBIRA JULY 29

Nyimbo Na. 49 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 26 ndime 16-22 ndi bokosi patsamba 209 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Machitidwe 26–28 (Mph. 10)

Na. 1: Machitidwe 26:19-32 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Akhristu Okhulupirika Adzatengedwa Kupita Kumwamba Mobisa Asanafe?—rs tsa. 215 ndime 2 mpaka tsa. 216 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Tingadziwe Bwanji Kuti Mzimu Woyera wa Mulungu Ukugwira Ntchito mwa Atumiki Ake?—Agal. 5:22, 23; Chiv. 22:17 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 96

Mph. 10: Kulankhula Mwachibadwa Polalikira. Nkhani yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 128 ndime 1, mpaka tsamba 129 ndime 1. Mwachidule, funsani wofalitsa mmodzi kuti afotokoze zimene zinamuthandiza kuthetsa manyazi mu utumiki.

Mph. 10: Bokosi la Mafunso. Nkhani yokambirana yokambidwa ndi mkulu.

Mph. 10: Sonyezani Kuti Ndinudi Ana a Atate Wanu Wakumwamba. (Mat. 5:43-45) Nkhani yochokera mu Buku Lapachaka la 2013, tsamba 89 ndime 3, mpaka tsamba 90 ndime 1, ndi tsamba 164 ndime 2. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene tikuphunzirapo.

Nyimbo Na. 80 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena