Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/13 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 26

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 26
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 26
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 8/13 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa August 26

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 26

Nyimbo Na. 101 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 28 ndime 1-7 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Aroma 13–16 (Mph. 10)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (Mph. 20)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 11

Mph. 10: “Alimbikitseni Kuti Aziyambitsa Maphunziro a Baibulo Loweruka Loyamba la Mwezi.” Nkhani. Pomaliza chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingayambitsire phunziro Loweruka loyamba m’mwezi wa September. Limbikitsani onse kuti adzayesetse kuyambitsa maphunziro a Baibulo.

Mph. 10: Njira Zolalikirira Uthenga Wabwino: Gawo la Kagulu ndi Gawo la Aliyense Payekha. Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera m’buku la Gulu tsamba 102 ndime 3 mpaka tsamba 104 ndime 1. Funsani mtumiki wa magawo kuti afotokoze zimene ofalitsa a mumpingomo angachite ngati akufuna kupatsidwa gawo lawolawo.

Mph. 10: Zifukwa Zosonyeza Kuti Ife si Aneneri Onyenga. Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera m’buku la Kukambitsirana tsamba 35 ndime 3 mpaka kumapeto kwa tsamba 37. Chitani chitsanzo cha mfundo imodzi ya patsamba 37.

Nyimbo Na. 116 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena