Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/13 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa September 30

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa September 30
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 30
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 9/13 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa September 30

MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 30

Nyimbo Na. 81 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 1 ndime 15-21 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Agalatiya 1-6 (Mph. 10)

Na. 1: Agalatiya 1:18-24 mpaka 2:1-10 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Pali Zipembedzo Zambiri?—rs tsa. 83 ndime 1-tsa. 84 ndime 2 (Mph. 5)

Na. 3: N’chifukwa Chiyani Yehova Ali Woyenera Kulambiridwa?—Chiv.  4:11 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 108

Mph. 10: “Amenewanso Muziwaganizira.” Nkhani yokambirana. Chitani chitsanzo chosonyeza mmene mungayambitsire phunziro Loweruka loyambirira m’mwezi wa October.

Mph. 10: Njira Zolalikirira Uthenga Wabwino—Kulalikira Kwa Anthu a Zinenero Zonse. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Gulu, tsamba 104, ndime 2, mpaka tsamba 105, ndime 3. Chitaninso chitsanzo.

Mph. 10: Musadere Nkhawa. (Mat. 6:31-33) Nkhani yokambirana yochokera mu Buku Lapachaka la 2013, patsamba 138, ndime 3, mpaka tsamba 139, ndime 3. Pemphani omvera kuti anene zimene aphunzira pa nkhaniyo.

Nyimbo Na. 40 and Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena