Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/13 tsamba 3
  • “Ndilandira Mabuku Anuwo, Inunso Mukalandira Athu”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ndilandira Mabuku Anuwo, Inunso Mukalandira Athu”
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mumayamikira Mabuku Athu?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2000
  • Gwiritsani Ntchito Mwanzeru Mabuku Athu Ofotokoza Baibulo
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2005
  • Tizigwiritsa Ntchito Mwanzeru Mabuku Ndiponso Magazini
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Kodi Likuoneka Bwanji?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 9/13 tsamba 3

“Ndilandira Mabuku Anuwo, Inunso Mukalandira Athu”

N’kutheka kuti tinakumanapo ndi anthu ena amene anatiuza mawu ngati amenewa. Ndiye popeza sitilandira mabuku a zipembedzo omwe amanena zabodza, kodi tingamuyankhe bwanji munthu woteroyo mozindikira? (Aroma 1:25) Tinganene kuti: “Zikomo kwambiri. Koma kodi kapepala kanuka [kapena magazini yanuyi] kakufotokoza kuti mavuto amene anthu akukumana nawo adzatha bwanji? [Yembekezani kuti ayankhe. Ngati anganene kuti yankho la funso lanulo mulipeza mukawerenga kapepala kakeko, mukumbutseni zoti inuyo munamufotokozera kaye zimene zili m’magazini athu musanapemphe kuti mumugawire. Kenako werengani kapena nenani mawu a pa lemba la Mateyu 6:9, 10.] Yesu ananena kuti Ufumu wa Mulungu udzachititsa kuti chifuniro chake chichitike padziko lapansi. Choncho mabuku a chipembedzo amene ndimawerenga ndi omwe amagogomezera za Ufumu wa Mulungu umenewo. Kodi ndingakusonyezeni m’Baibulo zinthu zina zimene Ufumu wa Mulungu udzachite?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena