Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/13 tsamba 3
  • Kodi Mudzachita Zotani pa Nthawi ya Holide?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mudzachita Zotani pa Nthawi ya Holide?
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Nkhani Yofanana
  • N’chifukwa Chiyani a Mboni za Yehova Sachita Nawo Maholide Ena?
    Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri
  • Yesetsani Kuti Muzilambira Mulungu M’njira Yovomerezeka
    Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni?
  • “Sitimamanidwa Kanthu!”
    Galamukani!—1993
  • Kodi Zikondwerero Zonse Zimasangalatsa Mulungu?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 10/13 tsamba 3

Kodi Mudzachita Zotani pa Nthawi ya Holide?

Nthawi ya maholide achipembedzo komanso aboma imakhala yabwino kulalikira chifukwa anthu ambiri amapezeka panyumba. Choncho mipingo ikulimbikitsidwa kuti ikonze dongosolo lodzalowa mu utumiki nthawi ya holide. Mukhoza kulengeza pa Msonkhano wa Utumiki ngati mpingo wakonza dongosolo lililonse lapadera lolowa mu utumiki pa nthawi ya holide. Mungachitenso bwino kulimbikitsa aliyense amene angakwanitse kumalowa nawo mu utumiki pa nthawiyi. N’zoona kuti nafenso timafunikira kupuma komanso kuchita zinthu zathu pa nthawi ya holide. Komabe tingachite bwino kupatula nthawi yolowa mu utumiki. Kuchita nawo utumiki pa nthawi ya holide kungakuthandizeni kuti mukhale wosangalala.—Mat. 11:29, 30.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena