Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/13 tsamba 2
  • “Tabwera Kuti . . . ”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Tabwera Kuti . . . ”
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Nkhani Yofanana
  • Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Muzikonzekera Mawu Oyamba
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Kugawira Buku Lakuti Baibulo Limaphunzitsa Chiyani
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 11/13 tsamba 2

“Tabwera Kuti . . . ”

Nthawi zambiri tikafika pakhomo la munthu, munthuyo amadabwa kuti ndife ndani, ndipo tabwera kudzatani. Ndiye kodi tinganene mawu ati kuti asatidabwe? Tikalonjerana, mwina tingayambe ndi mawu akuti, “Tabwera kuti . . . ” Mwachitsanzo tinganene kuti: “Tabwera kuti tikambirane za vuto limene likudetsa nkhawa anthu ambiri kudera lathu lino. Kodi mukuganiza kuti . . . ” Kapena tinganene kuti, “Tabwera kuti tikusonyezeni mmene timaphunzirira Baibulo ndi anthu kwaulere.” Tikamanena mwamsanga chifukwa chimene tafikira pakhomo la anthu, anthuwo angakhale ndi chidwi chomvetsera zimene tikufuna kuwauza.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena