Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/14 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 10

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 10
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 10
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 2/14 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa February 10

MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 10

Nyimbo Na. 38 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 7 ndime 7-13 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Genesis 25-28 (Mph. 10)

Na. 1: Genesis 25:19-34 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Anthu Oukitsidwa Kuti Akalamulire ndi Khristu Adzakhala Ngati Iyeyo—rs tsa. 109 ndime 4-8 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Yehova Amaiona Bwanji Nkhani Yopembedza Mafano?—bh tsa. 154-156 ndime 1-5 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 94

Mph. 15: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Yohane 4:6-26 ndipo kambiranani mmene mavesiwa angatithandizire mu utumiki. Kambirananinso nkhani yakuti, “Zochitika mu Utumiki Wakumunda” patsamba 4.

Mph. 15: “Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Lembani Zokhudza Anthu Achidwi.” Nkhani yokambirana. Mukamakambirana kadontho kalikonse komwe kali pansi pa kamutu kakuti, “Kodi Tingachite Bwanji Zimenezi?” pemphani omvera kuti afotokoze chifukwa chake kugwiritsa ntchito mfundo imeneyo, n’kofunika.

Nyimbo Na. 98 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena