Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/14 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 24

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 24
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 24
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 2/14 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa February 24

MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 24

Nyimbo Na. 6 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 8 ndime 1-7 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Genesis 32-35 (Mph. 10)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (Mph. 20)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 96

Mph. 5: Yambitsani Phunziro la Baibulo Loweruka Loyambirira. Nkhani. Fotokozani zimene mpingo wanu udzachite zokhudza utumiki wakumunda Loweruka loyamba m’mwezi wa March. Chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingayambitsire phunziro pogwiritsa ntchito chitsanzo chomwe chili patsamba 4.

Mph. 15: Kufunika Kochita Khama. Nkhani yochokera mu Buku Lapachaka la 2013, tsamba 45, ndime 1, mpaka tsamba 46 ndime 1, komanso tsamba 136 mpaka 137. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene tikuphunzirapo.

Mph. 10: “Ntchito Yogawira Timapepala Toitanira Anthu ku Chikumbutso Idzayamba pa March 22.” Nkhani yokambidwa ndi woyang’anira utumiki. Perekani timapepala toitanira anthu ku Chikumbutso kwa onse, ndipo kambiranani zomwe zili m’kapepalako. Tchulani mfundo zimene zingagwire ntchito pa mpingo wanu, zimene zili m’kalata ya malangizo yopita kwa akulu, ndipo fotokozani zimene mpingo wakonza, kuti mudzathe kugawira timapepalati m’gawo lanu lonse.

Nyimbo Na. 109 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena