Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/14 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 24

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 24
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 24
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 3/14 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa March 24

MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 24

Nyimbo Na. 4 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 9 ndime 8-13 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Genesis 47-50 (Mph. 10)

Na. 1: Genesis 48:17-22 ndi 49:1-7 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Zochitika Zosonyeza Kukhalapo kwa Khristu Zimatenga Nyengo ya Zaka Zambiri—rs tsa. 162 ndime 1-2 (Mph. 5)

Na. 3: Kudzikuza Kumabweretsera Mavuto—Miy. 11:2; 1 Pet. 5:5-7 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 56

Mph. 10: Tsanzirani Nehemiya. Nkhani yokambirana. Pemphani omvera kuti afotokoze mmene chitsanzo cha Nehemiya chingatithandizire pa ntchito yathu yolalikira.

Mph. 10: Muzigwiritsa Ntchito Mafunso Kuti Muziphunzitsa Mogwira Mtima—Gawo 1. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki tsamba 236 mpaka 237 ndime 2. Chitani chitsanzo chachidule chosonyeza mfundo imodzi ya m’nkhaniyi.

Mph. 10: Yehova Amamva Pembedzero la Anthu Olungama. (1 Pet. 3:12) Nkhani yokambirana yochokera mu Buku Lapachaka la 2013, tsamba 66 ndime 1 mpaka 3 komanso tsamba 104 ndi 105. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene tikuphunzirapo.

Nyimbo Na. 6 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena