Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/14 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 31

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 31
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 31
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 3/14 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa March 31

MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 31

Nyimbo Na. 70 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 9 ndime 14-19 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Ekisodo 1-6 (Mph. 10)

Na. 1: Ekisodo 2:1-14 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kubweranso kwa Khristu Kudzakhala Kosaoneka—rs tsa. 162 ndime 3–tsa. 163 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Kutsutsana ndi Anthu Osankhidwa Ndi Mulungu Kuli Ngati Kutsutsana Ndi Yehova—lv tsa. 43-44 ndime 15-17 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 63

Mph. 10: “Njira Zosiyanasiyana Zogawirira Magazini Akale.” Nkhani yokambirana. Dziwitsani mpingo za magazini akale amene alipo oti ofalitsa angathe kukagawira mu utumiki. Pemphani omvera kuti afotokoze zosangalatsa zomwe zinachitika atagawira magazini akale. Pomaliza, funsani woyang’anira utumiki kuti afotokoze mmene ntchito yogawira timapepala toitanira anthu ku Chikumbutso ikuyendera.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Mateyu 28:20 komanso 2 Timoteyo 4:17. Kambiranani mmene malemba amenewa angatithandizire mu utumiki wathu.

Nyimbo Na. 135 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena