Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/14 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 16

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 16
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 16
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 6/14 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa June 16

MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 16

Nyimbo Na. 77 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 12 ndime 20-25 ndi bokosi patsamba 151 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Levitiko 6-9 (Mph. 10)

Na. 1: Levitiko 8:18-30 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Chifukwa Chimene Sitipemphera kwa “Oyera Mtima”—rs tsa. 332 ndime 2-4 (Mph. 5)

Na. 3: N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuvala Bwino Tikamachita Utumiki Wakumunda Kapena Kumisonkhano Yachikhristu?—lv tsa. 57 ndime 14-15 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 110

Mph. 30: “Kodi Mukudziwa Zimene Mungasankhe?” Mafunso ndi mayankho. Gwiritsani ntchito mfundo zomwe zili m’ndime yoyamba ngati mawu oyamba ndipo zimene zili m’ndime yachitatu ngati mawu omaliza. Mukambiranenso tsamba 215 mpaka 217 m’buku la Chikondi cha Mulungu. Limbikitsani ofalitsa onse obatizidwa kuti akamayenda, nthawi zonse azitenga khadi la DPA. Ikambidwe ndi mkulu woyenerera.

Nyimbo Na. 120 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena