Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/14 tsamba 5
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 23

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 23
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 23
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 6/14 tsamba 5

Ndandanda ya Mlungu wa June 23

MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 23

Nyimbo Na. 112 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 13 ndime 1-7 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Levitiko 10-13 (Mph. 10)

Na. 1: Levitiko 12:1-8 mpaka 13:1-8 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Zoona Zake za Kulambira Zinthu Zakale ndi Zifanizo za “Oyera Mtima”—rs tsa. 333 ndime 1–tsa. 334 ndime 2 (Mph. 5)

Na. 3: Yehova Amadana ndi Mawu Otukwana—lv tsa. 136-137 ndime 9-12 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 82

Mph. 10: Mabuku Ogawira M’mwezi wa July. Nkhani yokambirana. Fotokozani mwachidule zimene zili m’timabukuto. Kenako chitani chitsanzo chimodzi kapena ziwiri zosonyeza mmene tingagawirire timabukuti.

Mph. 20: “Kodi Tingathandize Bwanji Anthu Omwe Sadziwa Kuwerenga Komanso Amene Amavutika Kuwerenga?” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 55 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena