Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/14 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 25

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 25
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 25
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 8/14 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa August 25

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 25

Nyimbo Na. 32 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 15 ndime 7-12 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Numeri 14-16 (Mph. 10)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (Mph. 20)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 96

Mph. 5: Zitsanzo za Zomwe Zinachitika.Pemphani wofalitsa mmodzi kapena awiri kuti achite chitsanzo chosonyeza zomwe zinachitikadi pamene ankauza ena za Ufumu molimba mtima. Kambiranani mwachidule lemba la Aheberi 6:11, 12, ndipo kenako tsindikani chifukwa chake tiyenera kuchita khama tikamalalikira za Ufumu wa Mulungu.

Mph. 10: Kuuza Ena za Ufumu—Gawo 1. Nkhani yokambidwa ndi mkulu yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 280, ndime 1 mpaka 4.

Mph. 15: Kuuza Ena za Ufumu—Gawo 2. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 280 ndime 5 mpaka tsamba 281 ndime 1. Chitani chitsanzo chosonyeza wofalitsa akuthandiza munthu kudziwa kuti Ufumu wa Mulungu ndi boma lenileni.

Nyimbo Na. 101 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena