Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/14 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 27

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 27
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 27
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 10/14 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa October 27

MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 27

Nyimbo Na. 101 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 3 ndime 11-18 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Deuteronomo 11-13 (Mph. 10)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (Mph. 20)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 45

Mph. 15: “Kodi Tingatani Kuti Tiziona Kuti Ntchito Yolalikira Ndi Yofunika Kwambiri?” Nkhani yokambirana. Chitani chitsanzo chosonyeza wofalitsa akugawira buku lakuti, Baibulo Limaphunzitsa Chiyani kapena kapepala kalikonse.

Mph. 15: Muzikonzekera Bwino Kuti Muzilalikira Modzipereka. Nkhani yokambirana yochokera mu Nsanja ya Olonda ya August 15, 2014, tsamba 14-15, ndime 14 mpaka 20. Pemphani omvera kuti anene nkhani kapena mafunso amene anthu a m’dera lanu amaganizira nthawi zambiri. Kodi tingathandize bwanji anthu amenewa tikamalalikira? Pemphani apainiya awiri kapena mwamuna ndi mkazi wake kuti achite chitsanzo chosonyeza mmene ofalitsa angagwiritsire ntchito ndime zimenezi kukonzekera ulaliki wogwira mtima kwa anthu a m’dera lanu. Ochita chitsanzochi angasankhe buku limene angagwiritse ntchito.

Nyimbo Na. 95 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena