Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/15 tsamba 5
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 29

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 29
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 29
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 6/15 tsamba 5

Ndandanda ya Mlungu wa June 29

MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 29

Nyimbo Na. 5 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 15 ndime 1-10 (30 min.)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Mafumu 3-6 (8 min.)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (20 min.)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: “Kumbukirani masiku akale”—Deut. 32:7.

Nyimbo Na. 118

15 min: Mabuku Ogawira mu July. Nkhani yokambirana. Kambiranani mfundo zimene zikupezeka m’mabuku amene tidzagawire mwezi umenewu. Kenako chitani chitsanzo chosonyeza wofalitsa akuthandiza munthu watsopano mmene angagawirire mabukuwo.

15 min: Muzigwiritsa Ntchito Buku Lapachaka la 2015. Nkhani yokambirana. Kambiranani mwachidule “Kalata Yochokera ku Bungwe Lolamulira.” Pemphani omvera kuti afotokoze zinthu zochititsa chidwi palipoti la padziko lonse. Pomaliza, limbikitsani anthu onse kuti ayesetse kuwerenga Buku Lapachaka mpaka kulimaliza.

Nyimbo Na. 108 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena