Ndandanda ya Mlungu wa September 28
MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 28
Nyimbo Na. 99 ndi Pemphero
Phunziro la Baibulo la Mpingo:
cl mutu 19 ndime 9-17 (30 min.)
Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:
Kuwerenga Baibulo: 2 Mafumu 23-25 (8 min.)
Na. 1: 2 Mafumu 23:8-15 (Osapitirira 3 min.)
Na. 2: Zimene Angelo Amachita Pokwaniritsa Cholinga cha Mulungu—bh tsa. 97-98 ndime 4-6 (5 min.)
Na. 3: Tumikirani Yehova Mokhulupirika—bh tsa. 144-145 ndime 1-4 (5 min.)
Msonkhano wa Utumiki:
Mutu wa Mwezi Uno: ‘Muzichitira umboni mokwanira za uthenga wabwino.’—Mac. 20:24.
10 min: Paulo ndi Anzake Anachitira Umboni Mokwanira ku Filipi. Nkhani yokambirana. Werengani Machitidwe 16:11-15. Kenako kambiranani mmene mavesi amenewa angatithandizire mu utumiki.
20 min: “Tizigwiritsa Ntchito Kabuku ka Uthenga Wabwino Pophunzitsa Anthu.” Mafunso ndi mayankho. Mukamaliza kukambirana ndime 3, chitani chitsanzo chokonzekeredwa bwino chosonyeza wofalitsa akugawira kabuku ka Uthenga Wabwino n’kukambirana ndi munthuyo ndime imodzi.
Nyimbo Na. 114 ndi Pemphero