Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/15 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 19

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 19
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 19
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 10/15 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa October 19

MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 19

Nyimbo Na. 80 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 20 ndime 8-15 (30 min.)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Mbiri 8-11 (8 min.)

Na. 1: 1 Mbiri 11:15-25 (Osapitirira 3 min.)

Na. 2: Pemphero Limathandiza Kwambiri​—bh tsa. 170-173 ndime 16-20 (5 min.)

Na. 3: Kodi Mkulu wa Angelo Ndi Ndani?​—bh tsa. 218-219 (5 min.)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: Khalani “ozikika mozama” ndiponso ‘okhazikika m’chikhulupiriro.’​—Akol. 2:6, 7.

Nyimbo Na. 83

20 min: “Kodi Tingatani Kuti Tiziwafika pa Mtima Anthu Amene Timaphunzira Nawo?” Mafunso ndi mayankho. Chitani zitsanzo ziwiri. M’chitsanzo choyamba, mwininyumba akunena kuti mwana wake anamwalira ndipo ali kumwamba. Ndiyeno wofalitsa akuwerenga lemba la Mlaliki 9:5 pofotokoza zimene zimachitika munthu akamwalira. Koma vesili silinamuthandize kwenikweni mwininyumbayo ndipo akutsutsa zimene wofalitsayo akufotokoza. M’chitsanzo chachiwiri, wofalitsayo akulankhula mwaluso kwambiri pofotokozera mwininyumbayo zakuti akufa adzauka ndipo akuwerenga naye lemba la Yohane 5:28, 29. Mwininyumbayo akuoneka kuti walimbikitsidwa kwambiri ndi lembali ndipo akumvetsera pamene wofalitsayo akulankhula.

10 min: Kaya Ndinu Wamkulu Kapena Mwana, Mukhoza Kukhala Chitsanzo Kwa Ena. (Afil. 3:17; 1 Tim. 4:12) Nkhani yokambirana yochokera mu Buku Lapachaka la 2015, tsamba 71 ndime 2 mpaka 72 ndime 5 komanso tsamba 76 ndi 77. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene tikuphunzirapo.

Nyimbo Na. 90 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena