Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 August tsamba 2
  • August 7-13

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • August 7-13
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 August tsamba 2

August 7-13

EZEKIELI 28-31

  • Nyimbo Na. 85 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yehova Anapereka Cholowa kwa Anthu Omwe Sankamulambira”: (10 min.)

    • Ezek. 29:18​—Mfumu Nebukadinezara sinalandire malipiro aliwonse pa ntchito yovuta imene inagwira yogonjetsa Turo (it-2 1136 ¶4)

    • Ezek. 29:19​—Mfumu Nebukadinezara inapita kukalanda zinthu za ku Iguputo ngati malipiro chifukwa chogonjetsa Turo (it-1 698 ¶5)

    • Ezek. 29:20​—Yehova anapereka cholowa kwa a Babulo chifukwa choti anachita zinthu zimene iyeyo ankafuna (g86 11/8 27 ¶4-5)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Ezek. 28:12-19​—Kodi zochita za mafumu a Turo zikufanana bwanji ndi zochita za Satana? (it-2 604 ¶4-5)

    • Ezek. 30:13, 14​—Kodi ulosi umenewu unakwaniritsidwa bwanji? (w03 7/1 32 ¶1-3)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ezek. 29:1-12

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Kukonzekera Ulaliki wa Mwezi Uno: (15 min.) Kukambirana “Zitsanzo za Ulaliki.” Pambuyo poonetsa vidiyo ya chitsanzo cha ulaliki iliyonse, kambiranani mfundo zikuluzikulu za m’vidiyoyo. Limbikitsani ofalitsa kuti pochita zitsanzo za ulaliki azitchulanso zinthu zimene anthu akuda nazo nkhawa zomwe zangochitika kumene m’deralo ndipo azigwiritsa ntchito kavidiyo kakuti Kodi Mungakonde Kumva Uthenga Wabwino? pogawira kabuku ka Uthenga Wabwino.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 82

  • Zofunika pampingo: (5 min.) Mukhoza kukambirana mfundo zimene tikuphunzira mu Buku Lapachaka. (yb17 35-36)

  • “Muzikhala ndi Makhalidwe Amene Mulungu Amasangalala Nawo​—Kudzichepetsa”: (10 min.) Nkhani yokambirana. Onetsani vidiyo yakuti Muzipewa Zinthu Zimene Zingawononge Khalidwe Lanu la Kukhulupirika​—Kunyada.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 5 ¶1-9

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 20 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena