Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 July tsamba 7
  • Kudzipereka kwa Mulungu N’kofunika Kuposa Kuchita Masewera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kudzipereka kwa Mulungu N’kofunika Kuposa Kuchita Masewera
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Ndiyenera Kuganizira Mfundo Ziti pa Nkhani ya Masewera?
    Zimene Achinyamata Amafunsa
  • Kuika Maseŵera m’Malo Ake Oyenera
    Galamukani!—1991
  • Kodi Ndiyenera Kuloŵa Timu Yamaseŵero?
    Galamukani!—1996
  • Kodi Ndiloŵe m’Timu Yasukulu?
    Galamukani!—1991
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 July tsamba 7

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Kudzipereka kwa Mulungu N’kofunika Kuposa Kuchita Masewera

Mtsikana wanyamula chosewerera tenesi, mnyamata wanyamula mpira, mnyamata wina wanyamula chibonga chosewerera besibo

Kodi kuchita masewera n’kofunika? Inde, koma si kofunika kwambiri tikayerekezera ndi kuchita zinthu zomwe zingatithandize kuti tikhale paubwenzi wabwino ndi Yehova. (1 Tim. 4:8) Choncho, n’zofunika kwambiri kuti Akhristu asamalole kuti masewera aziwalepheretsa kuchita zinthu zauzimu.

ONERANI VIDIYO YAKUTI ZIMENE MUYENERA KUDZIWA PA NKHANI YOCHITA MASEWERA, KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  1. Anyamata akupalasa bwato

    1. Kodi tingaphunzire maluso ati tikamachita masewera?

  2. Mnyamata wakwiriridwa ndi zida zosewerera masewera onse omwe amakonda

    2. Kodi ndi mfundo ziti zomwe zingatithandize kudziwa ngati masewera enaake ali abwino kapena ayi?

  3. Mtsikana wokwiya wavala zovala zake zochitira masewera a nkhonya

    3. Kodi lemba la Salimo 11:5 lingatithandize bwanji kusankha masewera abwino?

  4. Mnyamata wokonda zampikisano komanso wodzimva akudzitamandira kuti amasewera bwino kuposa anzake

    4. Kodi tingagwiritse ntchito bwanji lemba la Afilipi 2:3 komanso la Miyambo 16:18 tikamachita masewera?

  5. Mtsikana akugona misonkhano ili m’kati

    5. Kodi lemba la Afilipi 1:10 lingatithandize bwanji kuti tisamawononge nthawi yathu yambiri tikuonera kapena kuchita masewera enaake?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena