Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 June tsamba 4
  • Achikulire Angatiphunzitse Zambiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Achikulire Angatiphunzitse Zambiri
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Muziona Kuti Achikulire Okhulupirika Ndi Amtengo Wapatali
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Yehova Amasamalira Mwachikondi Atumiki Ake Okalamba
    Nsanja ya Olonda—2008
  • Muziona Kuti Achinyamata Ndi Amtengo Wapatali
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Yehova Amakwaniritsa Zomwe Walonjeza
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 June tsamba 4
M’bale wachikulire akuonetsa zithunzi banja lachinyamata.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 48-50

Achikulire Angatiphunzitse Zambiri

48:21, 22; 49:1; 50:24, 25

Achikulire amalimbitsa chikhulupiriro chathu mwa Yehova komanso zimene anatilonjeza, akamatiuza ‘ntchito zodabwitsa’ zimene aona Yehovayo akuchita m’masiku otsiriza ano. (Sal. 71:17, 18) Ngati muli ndi mwayi wokhala ndi achikulire mumpingo wanu, afunseni

  • mmene Yehova wawathandizira kuthana ndi mavuto omwe akhala akukumana nawo pomutumikira

  • mmene amamvera akaona kuwonjezereka kwa olalikira Ufumu

  • mmene amasangalalira akaona momwe gulu lathu likufotokozera choonadi cha m’Baibulo momveka bwino masiku ano

  • zokhudza kusintha kumene aona kukuchitika m’gulu la Yehova

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena