Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 June tsamba 6
  • June 22-28

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • June 22-28
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 June tsamba 6

June 22-28

EKISODO 1–3

  • Nyimbo Na. 7 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Ndidzakhala Amene Ndidzafune Kukhala”: (10 min.)

    • [Onerani vidiyo ya Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Ekisodo.]

    • Eks. 3:13​—Mose ankafuna kudziwa tanthauzo la dzina la Yehova komanso kuti iye ndi ndani kwenikweni (w13 3/15 25 ¶4)

    • Eks. 3:14​—Yehova amakhala chilichonse chomwe chingafunikire kuti akwaniritse cholinga chake (kr 43, bokosi)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Eks. 2:10​—N’chifukwa chiyani tinganene kuti mwana wamkazi wa Farao ndi amene anatenga Mose n’kumamulera? (g04 4/8 22 ¶2)

    • Eks. 3:1​—Kodi Yetero anali wansembe wotani? (w04 3/15 24 ¶4)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Eks. 2:11-25 (th phunziro 11)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Sonyezani mmene mungayankhire munthu amene wanena zinthu zina zomwe anthu amakonda kunena ngati sakufuna kuti tikambirane nawo. (th phunziro 16)

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza. Kenako gawirani magazini ya posachedwapa imene ili ndi nkhani yomwe mwininyumba anayambitsa. (th phunziro 12)

  • Nkhani: (Osapitirira 5 min.) w02 6/15 11 ¶1-4​—Mutu: Chinthu Choposa Chuma cha Aigupto. (th phunziro 13)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 2

  • Khalani Bwenzi La Yehova​—Dzina la Yehova: (6 min.)

  • Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako itanani ana amene munawasankhiratu kuti abwere kutsogolo ndipo muwafunse mafunso otsatirawa: Kodi dzina lakuti Yehova limatanthauza chiyani? Kodi Yehova analenga chiyani? Kodi Yehova angakuthandizeni bwanji?

  • Dzina la Mulungu Linakwezedwa ku Scandinavia: (9 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: N’chifukwa chiyani anthu ochepa okha ndi amene ankadziwa dzina la Mulungu zisanafike zaka za m’ma 1500? Kodi dzina la Yehova linayamba bwanji kugwiritsidwa ntchito ku Scandinavia? N’chifukwa chiyani mumaona kuti Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika ndi lamtengo wapatali?

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 88 ndime 12-19

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

• Nyimbo Na. 49 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena