Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 July tsamba 14
  • Muzikhala Okhulupirika kwa Yehova Mukamasankha Anthu Ocheza Nawo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzikhala Okhulupirika kwa Yehova Mukamasankha Anthu Ocheza Nawo
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Zimene Tikuphunzira kwa Nehemiya
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Mwapatulidwa
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Muzilimbikitsa Abale ndi Alongo Anu Akakumana ndi Mavuto
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • “Chimwemwe Chimene Yehova Amapereka Ndicho Malo Anu Achitetezo”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 July tsamba 14
Nehemiya akutaya katundu wa Tobiya yemwe anali m’chipinda chodyera cha m’kachisi.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Muzikhala Okhulupirika kwa Yehova Mukamasankha Anthu Ocheza Nawo

Aamoni komanso Amowabu sankaloledwa ‘kulowa mumpingo’ chifukwa anali ndi mbiri yoti ankatsutsa anthu a Mulungu (Ne 13:1, 2; it-1 95 ¶5)

Mkulu wa Ansembe Eliyasibu analola munthu wa Chiamoni kuti azigwiritsa ntchito chipinda chodyera cha m’kachisi (Ne 13:4, 5; w13 8/15 4 ¶5-6)

Nehemiya anasonyeza kuti anali wokhulupirika kwa Yehova mwa kuthetsa mgwirizano umene unalipo pakati pa Eliyasibu ndi mdani wa Mulungu (Ne 13:7-9)

Kodi tingakhale okhulupirika kwa Yehova ngati timacheza ndi anthu amene samutumikira?​—w96 3/15 16 ¶6.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi Yehova amamva bwanji akaona anthu amene ndimasankha kucheza nawo?’

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena