Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb24 March tsamba 8
  • March 25-31

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • March 25-31
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2024
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2024
mwb24 March tsamba 8

MARCH 25-31

SALIMO 22

Nyimbo Na. 19 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Msilikali wa Chiroma akuona malaya akunja a Yesu pomwe asilikali ena awiri akuchita maere pa malayawo.

Asilikali akuchita maere pa malaya akunja a Yesu.

1. Baibulo Linaneneratu Zinthu Zina Zokhudza Imfa ya Yesu

(10 min.)

Anthu adzaona ngati Yesu wasiyidwa ndi Mulungu (Sl 22:1; w11 8/15 15 ¶16)

Yesu adzanyozedwa (Sl 22:7, 8; w11 8/15 15 ¶13)

Adzachita maere pa zovala za Yesu (Sl 22:18; w11 8/15 15 ¶14; onani chithunzi chapachikuto)

Mlongo wakhala pansi pamtengo m’Paradaiso limodzi ndi mkango wa m’phiri ndipo ana a nyama zotchedwa llama akudya msipu pafupi naye.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi Salimo 22 lalimbitsa bwanji chikhulupiriro changa choti maulosi ena okhudza Mesiya, monga wopezeka pa Mika 4:4, adzakwaniritsidwa?’

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Sl 22:22​—Kodi masiku ano tingatsanzire wolemba masalimo m’njira ziwiri ziti? (w06 11/1 29 ¶7; w03 9/1 20 ¶1)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Sl 22:1-19 (th phunziro 2)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(3 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. (lmd phunziro 4 mfundo 4)

5. Ulendo Wobwereza

(4 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Chitani ulendo wobwereza kwa mnzanu amene analandira kapepala komuitanira ku Chikumbutso. (lmd phunziro 4 mfundo 3)

6. Nkhani

(5 min.) w20.07 12-13 ¶14-17​—Mutu: Kodi Maulosi a M’Baibulo Amatithandiza Bwanji Kukhala ndi Chikhulupiriro Cholimba? (th phunziro 20)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 95

7. Zofunika Pampingo

(15 min.)

8. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) bt mutu 7 ¶14-18, bokosi patsamba 57-58

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 53 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena