Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb24 July tsamba 3
  • July 8-14

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • July 8-14
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2024
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2024
mwb24 July tsamba 3

JULY 8-14

MASALIMO 60-62

Nyimbo Na. 2 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Zithunzi: 1. Bambo akuthamangira ku nsanja yolimba. 2. Bambo akumwetulira ndipo akulozera anthu ku tenti yake kumene anthu ena akudya chakudya. 3.Thanthwe.

1. Yehova Amatiteteza

(10 min.)

Yehova ali ngati nsanja yolimba (Sl 61:3; it-2 1118 ¶7)

Yehova amatilola kuti tikhale alendo mutenti yake (Sl 61:4; it-2 1084 ¶8)

Yehova ali ngati thanthwe (Sl 62:2; w02 4/15 16 ¶14)


DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi moyo wanga wasintha bwanji chifukwa chakuti ndinadziwa Yehova komanso ndimamudalira?’

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Sl 62:11—Kodi “mphamvu ndi za Mulungu” m’njira yotani? (w06 6/1 11 ¶8)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Sl 60:1–61:8 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(3 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Yambani kukambirana ndi munthu amene wakusonyezani kukoma mtima. (lmd phunziro 2 mfundo 3)

5. Ulendo Wobwereza

(4 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Muuzeni za JW Library® ndipo musonyezeni mmene angaiikire muchipangizo chake. (lmd phunziro 7 mfundo 4)

6. Nkhani

(5 min.) w22.02 4-5 ¶7-10—Mutu: Muzikhulupirira Yehova Mukapatsidwa Malangizo. (th phunziro 20)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 12

7. Palibe Chimene ‘Chidzatilekanitse ndi Chikondi cha Mulungu’

(10 min.) Nkhani yokambirana.

Onerani VIDIYO. Kenako funsani omvera funso ili:

  • Kodi Yehova anasamalira bwanji M’bale Nyirenda pamene ankazunzidwa?

8. Khalani Bwenzi la Yehova—Zomwe Uyenera Kuchita Kuti Ubatizidwe

(5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani VIDIYO. Kenako ngati n’zotheka itanani ana amene munawasankhiratu kuti abwere papulatifomu ndipo afunseni mafunso awa: Kuti munthu abatizidwe, kodi chofunika kwambiri ndi zaka zake? Fotokozani. Kodi munthu ayenera kuchita zinthu ziti kuti abatizidwe?

9. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) bt mutu 12 ¶7-13, bokosi patsamba 97

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 63 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena