NOVEMBER 25–DECEMBER 1
MASALIMO 109-112
Nyimbo Na. 14 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)
1. Muzithandiza Yesu, Mfumu Yathu
(10 min.)
Atapita kumwamba, Yesu anakhala kudzanja lamanja la Yehova (Sl 110:1; w06 9/1 13 ¶6)
Mu 1914, Yesu anayamba kugonjetsa adani ake (Sl 110:2; w00 4/1 18 ¶3)
Tingadzipereke mofunitsitsa pothandiza ulamuliro wa Yesu (Sl 110:3; be 76 ¶2)
DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndingakhale ndi zolinga zotani pofuna kusonyeza kuti ndimathandiza Ufumu wa Mulungu?’
2. Mfundo Zothandiza
(10 min.)
Sl 110:4—Fotokozani pangano lomwe lili muvesili. (it-1 524 ¶2)
Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?
3. Kuwerenga Baibulo
(4 min.) Sl 109:1-26 (th phunziro 2)
4. Ulendo Woyamba
(2 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Yambani kukambirana pogwiritsa ntchito kapepala. (lmd phunziro 4 mfundo 3)
5. Kufotokoza Zimene Mumakhulupirira
(5 min.) Chitsanzo. ijwfq 23—Mutu: N’chifukwa Chiyani a Mboni za Yehova Samenya Nawo Nkhondo? (lmd phunziro 4 mfundo 4)
6. Kuphunzitsa Anthu
Nyimbo Na. 72
7. Kodi Tingathandize Bwanji Ufumu wa Mulungu Mokhulupirika?
(15 min.) Nkhani yokambirana.
Ufumu wa Mulungu umasonyeza kuti Yehova ndi wolamulira wachilengedwe chonse. (Da 2:44, 45) Choncho nthawi zonse tikamachita zinthu zothandiza Ufumu wa Mulungu, timakhala tikusonyeza kuti Yehova ndi wolamulira wabwino.
Onerani VIDIYO yakuti Muzithandiza “Kalonga Wamtendere” Mokhulupirika. Kenako funsani funso ili:
Kodi timathandiza bwanji Ufumu wa Mulungu mokhulupirika?
Lembani lemba lomwe likugwirizana ndi njira zotsatirazi za mmene tingathandizire Ufumu wa Mulungu.
Kuona kuti Ufumuwu ndi wofunika kwambiri pa moyo wathu.
Kukhala ndi makhalidwe abwino omwe nzika za Ufumuwu zimayenera kukhala nawo.
Kuuza ena mwakhama zokhudza Ufumu.
Kulemekeza maboma a anthu, koma kumvera Mulungu ngati malamulo a Kaisara akutsutsana ndi malamulo a Mulungu.
8. Phunziro la Baibulo la Mpingo
(30 min.) bt mutu 18 ¶16-24