Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb26 March tsamba 2
  • March 2-8

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • March 2-8
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2026
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2026
mwb26 March tsamba 2

MARCH 2-8

YESAYA 41-42

Nyimbo Na. 8 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. “Usachite Mantha”

(10 min.)

Yehova adzapatsa mphamvu “winawake kuchokera kotulukira dzuwa,” yemwe adzachititse anthu kunjenjemera (Yes 41:​2, 5; ip-2 21 ¶10-mwbr)

Anthu amene ankalambira Yehova sankafunika kuchita mantha (Yes 41:10; ijwbv nkhani na. 5 ¶4-7-mwbr)

Yehova akanawathandiza (Yes 41:13)


FUNSO LOFUNIKA KULIGANIZIRA: Kodi ulosi wa mu Yesaya chaputala 41, umathandiza bwanji Akhristu masiku ano?—w16.07 18 ¶4-5-mwbr.

Banja limene likukhala m’dziko lomwe ntchito yathu ndi yoletsedwa likuphunzira Baibulo. Bambo ali tcheru ndipo akuyang’ana pawindo pomwe mayi akuwerenga Baibulo limodzi ndi ana awo awiri.

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Yes 41:8—Kodi Yehova anasonyeza bwanji kuti Abulahamu anali mnzake? (w01 10/1 20 ¶3-mwbr)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Yes 42:​1-13 (th phunziro 11)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(3 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Mwininyumba walandira kapepala komuitanira ku Chikumbutso ndipo wasonyeza chidwi kuti adzapita. (lmd phunziro 6, mfundo 4)

5. Ulendo Woyamba

(4 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Itanirani wachibale kumwambo wa Chikumbutso ndipo gwiritsani ntchito jw.org kuti mupeze malo a kufupi ndi kwawo, komwe kukachitikire mwambowu. (lmd phunziro 3, mfundo 5)

6. Kufotokoza Zimene Mumakhulupirira

(5 min.) Nkhani. ijwbq nkhani na. 60—Mutu: Kodi Mungatani Kuti Musamaope Kwambiri Imfa? (th phunziro 1)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 19

7. Ntchito Yoitanira Anthu ku Chikumbutso Iyamba Loweruka pa 7 March

(5 min.) Nkhaniyi ikambidwe ndi woyang’anira utumiki. Fotokozani zimene mpingo wanu wakonza zokhudza ntchitoyi, nkhani yapadera komanso mwambo wa Chikumbutso. Limbikitsani onse kuti ayesetse kuchita zambiri mu utumiki m’miyezi ya March ndi April. Ofalitsa angachite upainiya wothandiza wa maola 15.

8. Vidiyo ya Zimene Gulu Lathu Lachita ya March

(10 min.) Nkhani yokambirana.

Onerani VIDIYOYI. Kenako funsani mafunso omwe aoneka muvidiyoyi.

9. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) lfb mutu 66-67

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 110 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena