Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb26 March tsamba 3
  • March 9-15

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • March 9-15
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2026
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2026
mwb26 March tsamba 3

MARCH 9-15

YESAYA 43-44

Nyimbo Na. 63 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Ulosi Umene Unalembedwa Kutatsala Zaka 200

(10 min.)

Asilikali akuwoloka mtsinje wa Firate ndipo akulowa pageti la mzinda wa Babulo lomwe alipeza losatseka.

Mitsinje ya Babulo ‘idzaumitsidwa’ (Yes 44:27; gm 123-124 ¶16-17-mwbr)

Koresi adzakhala ngati “m’busa” wa Mulungu pogonjetsa Babulo (Yes 44:28a; it-E “Koresi” ¶7-mwbr)

Koresi adzatumiza anthu a Mulungu kuti akamangenso mzinda komanso kachisi (Eza 1:​1-3; Yes 44:28b; it-E “Koresi” ¶17-mwbr)


FUFUZANI: Kodi Koresi anakwaniritsa bwanji ulosi wa pa Yesaya 45:​1-4?

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Yes 44:28—Kodi tikudziwa bwanji kuti Yehova sanakakamize Koresi kuti azimulambira? (w24.02 30 ¶8-mwbr)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Yes 44:​9-20 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(1 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Mugawireni kapepala koitanira anthu ku Chikumbutso. (lmd phunziro 4, mfundo 3)

5. Ulendo Woyamba

(3 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Itanirani mnzanu kumwambo wa Chikumbutso. (lmd phunziro 3, mfundo 4)

6. Ulendo Woyamba

(3 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Pemphani abwana anu kuti patsiku la Chikumbutso adzakuloleni kuti musadzagwire ntchito. (lmd phunziro 6, mfundo 3)

7. Ulendo Wobwereza

(4 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Pemphani munthu amene pa ulendo wapita analandira kapepala koitanira anthu ku Chikumbutso kuti muziphunzira naye Baibulo. (lmd phunziro 7, mfundo 4)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 69

8. Zofunika Pampingo

(15 min.)

9. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) ) lfb mawu oyamba a gawo 11 ndi mutu 68-69

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 137 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena