Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb26 March tsamba 10
  • April 6-12

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • April 6-12
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2026
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2026
mwb26 March tsamba 10

APRIL 6-12

YESAYA 50-51

Nyimbo Na. 88 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Muzimvera Yesu Yemwe Anaphunzitsidwa ndi Yehova

(10 min.)

Yesu anaphunzitsidwa ndi Yehova asanabwere padziko lapansi (Yes 50:4; kr 182 ¶5-mwbr)

Yesu ankafunitsitsa kuphunzira (Yes 50:5; cf 133 ¶13-mwbr)

Anthu amene amaopa Yehova amamvera mawu a Mtumiki wake Yesu (Yes 50:10; Yoh 10:27)

Yesu akulankhula ndi gulu la anthu pafupi ndi nyanja.

FUNSO LOFUNIKA KULIGANIZIRA: Kodi tingatsanzire bwanji Yesu pa nkhani yokhala wofunitsitsa kuphunzitsidwa ndi Yehova?—1Pet 2:21.

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Yes 51:1—Kodi vesili likutanthauza chiyani? (it-E “Malo Okumbapo Miyala” ¶2-mwbr)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Yes 50:​1-11 (th phunziro 2)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(3 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Fotokozerani mnzanu wakuntchito zokhudza Chikumbutso. (lmd phunziro 2, mfundo 4)

5. Ulendo Wobwereza

(4 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Itanirani mwininyumba yemwe anapezeka ku Chikumbutso kumisonkhano yotsatira. (lmd phunziro 9, mfundo 4)

6. Kufotokoza Zimene Mumakhulupirira

(5 min.) Chitsanzo. ijwbq nkhani na. 140 ¶4—Mutu: Kodi Kungokhulupirira Yesu N’kokwanira Kuti Tidzapulumuke? (lmd phunziro 11, mfundo 5)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 99

7. Zofunika Pampingo

(15 min.)

8. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) ) lfb mawu oyamba a gawo 12 komanso mutu 74-75

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 13 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena