Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb26 March tsamba 11-16
  • April 13-19

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • April 13-19
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2026
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2026
mwb26 March tsamba 11-16

APRIL 13-19

YESAYA 52-53

Nyimbo Na. 18 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

[Chithunzi chapachikuto]

Yesu akupita kukaphedwa

1. Yesu Anatisonyeza Chikondi Chachikulu

(10 min.)

Yesaya analosera kuti Yesu adzanyozedwa (Yes 53:3; Mt 26:​67, 68; w10 11/15 7 ¶2-mwbr)

Yesu analola kuti azunzidwe (Yes 53:7; ip-2 205 ¶25-mwbr)

Chifukwa cha chikondi, Yesu anali wofunitsitsa kuvutika kuti achite zimene Yehova ankafuna komanso kunyamula machimo athu (Yes 53:​10-12; Yoh 14:31; 15:13)

Yesu, wavindikiridwa nkhope ndipo wazunguliridwa ndi atsogoleri achipembedzo. Mmodzi wa atsogoleriwo akumumenya pomwe enawo akumunyoza.

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Yes 52:11—Kodi Aisiraeli akanatsatira bwanji lamulo la mu ulosiwu, nanga ifeyo tingalitsatire bwanji? (it-E “Ziwiya” ¶2-mwbr)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Yes 53:​3-12 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(4 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Pemphani mwininyumba kuti muziphunzira naye Baibulo. (lmd phunziro 4, mfundo 4)

5. Ulendo Woyamba

(3 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Kambiranani mfundo imodzi ya choonadi mu Zakumapeto A, m’kabuku kakuti Muzikonda Anthu. (lmd phunziro 3, mfundo 3)

6. Ulendo Wobwereza

(5 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Pemphani munthu amene anapezeka pa Chikumbutso kuti muziphunzira naye Baibulo. (lmd phunziro 8, mfundo 3)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 20

7. Khalani Bwenzi la Yehova—Anasonyeza Chikondi Chachikulu Kwambiri

(15 min.) Nkhani yokambirana.

Chithunzi cha muvidiyo yakuti “Khalani Bwenzi la Yehova​—⁠Anasonyeza Chikondi Chachikulu Kwambiri.” Yesu monga Mfumu yomwe ili kumwamba.

Onerani VIDIYO. Kenako funsani funso ili:

  • Kodi nsembe ya Yesu ndi mphatso m’njira yotani?

  • Kodi tingasonyeze bwanji kuti timayamikira nsembe yake?

8. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) lfb mutu 76-77

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 57 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena