Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • ijwbq nkhani 4
  • Kodi Mose Ndi Amene Analemba Baibulo?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mose Ndi Amene Analemba Baibulo?
  • Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Yankho la m’Baibulo
  • Mmene Moyo wa Mose Umakukhudzirani
    Galamukani!—2004
  • Phunzirani Njira za Yehova
    Nsanja ya Olonda—2005
  • Kodi Ndimotani Mmene Yesu Kristu Analiri Mneneri Wofanana ndi Mose?
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Mose Anali Munthu Wachikondi
    Nsanja ya Olonda—2013
Onani Zambiri
Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
ijwbq nkhani 4
Mose wanyamula miyala yosema

Kodi Mose Ndi Amene Analemba Baibulo?

Yankho la m’Baibulo

Mulungu anagwiritsira ntchito Mose polemba mabuku asanu oyambirira a m’Baibulo. Mabuku ake ndi: Genesis, Ekisodo, Levitiko, Numeri ndiponso Deuteronomo. Zikuonekanso kuti Mose ndi amene analemba buku la Yobu ndi Salimo 90. Koma Mose anali m’modzi mwa anthu 40 amene Mulungu anawagwiritsira ntchito polemba Baibulo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena