Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • ijwbq nkhani 8
  • Kodi Mulungu Ali ndi Malo Enieni Amene Amakhala?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mulungu Ali ndi Malo Enieni Amene Amakhala?
  • Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Yankho la m’Baibulo
  • Kodi Mulungu Ali Ndi Malo Enieni Amene Amakhala?
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Kodi Mulungu Ali Paliponse?
    Galamukani!—2005
  • Kodi Kumwamba N’kotani?
    Nsanja ya Olonda—2010
  • Kodi Mulungu Ali Paliponse?
    Galamukani!—2011
Onani Zambiri
Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
ijwbq nkhani 8
Dzuwa likulowa

Kodi Mulungu Ali ndi Malo Enieni Amene Amakhala?

Yankho la m’Baibulo

Inde. Mulungu ali ndi malo enieni amene amakhala ndipo ndi kumwamba. Taonani mavesi a m’Baibulo otsatirawa:

Popemphera, Mfumu Solomo anati: “Inuyo mumve muli kumwamba, malo anu okhala okhazikika.”—1 Mafumu 8:43.

Yesu Khristu anauza ophunzira ake kuti azipemphera kwa ‘Atate wawo wakumwamba.’—Mateyu 6:9.

Yesu ataukitsidwa, “analowa kumwamba kwenikweniko. Tsopano ali kumwamba kuti aonekere pamaso pa Mulungu.”—Aheberi 9:24.

Mavesiwa akusonyeza kuti Yehova Mulungu ndi munthu weniweni ndipo sakhala paliponse koma amakhala kumwamba.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena