Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • nwt tsamba 1846-1848
  • Zimene Zili Mʼbuku la Machitidwe

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Zili Mʼbuku la Machitidwe
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Nkhani Yofanana
  • Lengezani Ufumu wa Yehova Molimba Mtima!
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Timoteo—Wothandiza Paulo
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
  • Pitani Patsogolo Mwauzimu Potsanzira Paulo
    Nsanja ya Olonda—2008
  • “Ndikuchita Apilo Kuti Ndikaonekere kwa Kaisara”
    ‘Kuchitira Umboni Mokwanira za Ufumu wa Mulungu’
Onani Zambiri
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Zimene Zili Mʼbuku la Machitidwe

MACHITIDWE

ZIMENE ZILI MʼBUKULI

  • 1

    • Mawu oyamba opita kwa Teofilo (1-5)

    • Kulalikira mpaka kumalekezero a dziko lapansi (6-8)

    • Yesu anapita kumwamba (9-11)

    • Ophunzira anasonkhana mogwirizana (12-14)

    • Matiya anasankhidwa kuti alowe mʼmalo mwa Yudasi (15-26)

  • 2

    • Anthu analandira mzimu woyera pa Pentekosite (1-13)

    • Nkhani imene Petulo anakamba (14-36)

    • Anthu anatsatira zimene Petulo ananena (37-41)

      • Anthu 3,000 anabatizidwa (41)

    • Akhristu ankachitira zinthu limodzi (42-47)

  • 3

    • Petulo anachiritsa munthu wolumala wopemphapempha (1-10)

    • Nkhani imene Petulo anakamba Pakhonde Lazipilala la Solomo (11-26)

      • “Nthawi yobwezeretsa zinthu zonse” (21)

      • Mneneri ngati Mose (22)

  • 4

    • Petulo ndi Yohane anamangidwa (1-4)

      • Amuna okhulupirira anakwana 5,000 (4)

    • Kuweruzidwa ndi Khoti Lalikulu la Ayuda (5-22)

      • “Ife sitingasiye kulankhula” (20)

    • Anapemphera kuti akhale olimba mtima (23-31)

    • Ophunzira ankagawana zinthu (32-37)

  • 5

    • Hananiya ndi Safira (1-11)

    • Atumwi anachita zizindikiro zambiri (12-16)

    • Anamangidwa nʼkumasulidwa (17-21a)

    • Anapita nawonso ku Khoti Lalikulu la Ayuda (21b-32)

      • ‘Kumvera Mulungu osati anthu’ (29)

    • Malangizo a Gamaliyeli (33-40)

    • Kulalikira kunyumba ndi nyumba (41, 42)

  • 6

    • Amuna 7 anasankhidwa kuti azitumikira (1-7)

    • Sitefano anaimbidwa mlandu wonyoza Mulungu (8-15)

  • 7

    • Zimene Sitefano ananena polankhula ndi Khoti Lalikulu la Ayuda (1-53)

      • Nthawi ya makolo akale (2-16)

      • Mose anali mtsogoleri; Aisiraeli ankalambira mafano (17-43)

      • Mulungu sakhala mu akachisi omangidwa ndi anthu (44-50)

    • Sitefano anaponyedwa miyala (54-60)

  • 8

    • Saulo ankazunza anthu (1-3)

    • Utumiki wa Filipo unkayenda bwino ku Samariya (4-13)

    • Petulo ndi Yohane anatumizidwa ku Samariya (14-17)

    • Simoni ankafuna kugula mzimu woyera (18-25)

    • Nduna ya ku Itiyopiya (26-40)

  • 9

    • Saulo ali pa ulendo wa ku Damasiko (1-9)

    • Hananiya anatumizidwa kuti akathandize Saulo (10-19a)

    • Saulo analalikira za Yesu ku Damasiko (19b-25)

    • Saulo anapita ku Yerusalemu (26-31)

    • Petulo anachiritsa Eneya (32-35)

    • Dolika, yemwe anali wopatsa, anaukitsidwa (36-43)

  • 10

    • Masomphenya a Koneliyo (1-8)

    • Masomphenya a Petulo a nyama zoyeretsedwa (9-16)

    • Petulo anapita kunyumba kwa Koneliyo (17-33)

    • Petulo analalikira uthenga wabwino kwa anthu a mitundu ina (34-43)

      • “Mulungu alibe tsankho” (34, 35)

    • Anthu a mitundu ina analandira mzimu woyera nʼkubatizidwa (44-48)

  • 11

    • Petulo anakapereka lipoti kwa atumwi (1-18)

    • Baranaba ndi Saulo anapita ku Antiokeya wa ku Siriya (19-26)

      • Ophunzira anayamba kutchedwa Akhristu (26)

    • Agabo analosera za njala (27-30)

  • 12

    • Yakobo anaphedwa; Petulo anamangidwa (1-5)

    • Petulo anamasulidwa modabwitsa (6-19)

    • Herode anaphedwa ndi mngelo (20-25)

  • 13

    • Baranaba ndi Saulo anatumizidwa kuti akakhale amishonale (1-3)

    • Utumiki wa ku Kupuro (4-12)

    • Zimene Paulo analankhula ku Antiokeya wa ku Pisidiya (13-41)

    • Ulosi woti ayambe kulalikira kwa anthu a mitundu ina (42-52)

  • 14

    • Okhulupirira anawonjezeka ku Ikoniyo; anayamba kutsutsidwa (1-7)

    • Ankawayesa kuti ndi milungu ku Lusitara (8-18)

    • Paulo anapulumuka atamuponya miyala (19, 20)

    • Analimbikitsa mipingo (21-23)

    • Anabwerera ku Antiokeya wa ku Siriya (24-28)

  • 15

    • Anatsutsana ku Antiokeya pa nkhani ya mdulidwe (1, 2)

    • Nkhaniyi anapita nayo ku Yerusalemu (3-5)

    • Akulu ndi atumwi anakumana kuti akambirane (6-21)

    • Kalata yochokera ku bungwe lolamulira (22-29)

      • Azipewa magazi (28, 29)

    • Mipingo inalimbikitsidwa ndi kalata (30-35)

    • Paulo ndi Baranaba anasiyana (36-41)

  • 16

    • Paulo anasankha Timoteyo (1-5)

    • Masomphenya a munthu wa ku Makedoniya (6-10)

    • Lidiya anakhala Mkhristu ku Filipi (11-15)

    • Paulo ndi Sila anamangidwa (16-24)

    • Woyangʼanira ndende ndi banja lake anabatizidwa (25-34)

    • Paulo ananena kuti akuluakulu a zamalamulo apepese (35-40)

  • 17

    • Paulo ndi Sila ku Tesalonika (1-9)

    • Paulo ndi Sila ku Bereya (10-15)

    • Paulo ku Atene (16-22a)

    • Zimene Paulo analankhula kubwalo la Areopagi (22b-34)

  • 18

    • Utumiki wa Paulo ku Korinto (1-17)

    • Anabwerera ku Antiokeya wa ku Siriya (18-22)

    • Paulo anachoka ku Galatiya ndi ku Fulugiya (23)

    • Apolo, yemwe ankalankhula mwaluso, anathandizidwa (24-28)

  • 19

    • Paulo ku Efeso; anthu ena anabatizidwanso (1-7)

    • Ntchito yolalikira ya Paulo (8-10)

    • Utumiki unkayenda bwino ngakhale kuti ena ankakhulupirira zamizimu (11-20)

    • Chisokonezo ku Efeso (21-41)

  • 20

    • Paulo ku Makedoniya ndi ku Girisi (1-6)

    • Utiko anaukitsidwa ku Torowa (7-12)

    • Kuchoka ku Torowa kupita ku Mileto (13-16)

    • Paulo anakumana ndi akulu a ku Efeso (17-38)

      • Ankaphunzitsa kunyumba ndi nyumba (20)

      • “Kupatsa kumatichititsa kukhala osangalala kwambiri” (35)

  • 21

    • Ulendo wa ku Yerusalemu (1-14)

    • Anafika ku Yerusalemu (15-19)

    • Paulo anatsatira malangizo a akulu (20-26)

    • Chisokonezo mʼkachisi; Paulo anamangidwa (27-36)

    • Paulo analoledwa kulankhula ndi gulu la anthu (37-40)

  • 22

    • Mawu a Paulo odziteteza pamaso pa gulu la anthu (1-21)

    • Paulo anagwiritsa ntchito mwayi wokhala nzika ya Roma (22-29)

    • Khoti Lalikulu la Ayuda linakumana (30)

  • 23

    • Paulo analankhula pamaso pa Khoti Lalikulu la Ayuda (1-10)

    • Paulo analimbikitsidwa ndi Ambuye (11)

    • Chiwembu chofuna kupha Paulo (12-22)

    • Paulo anapititsidwa ku Kaisareya (23-35)

  • 24

    • Milandu imene Paulo ankaimbidwa (1-9)

    • Paulo anadziteteza pamaso pa Felike (10-21)

    • Mlandu wa Paulo unaimitsidwa kwa zaka ziwiri (22-27)

  • 25

    • Mlandu wa Paulo pamaso pa Fesito (1-12)

      • “Ndikuchita apilo kuti ndikaonekere kwa Kaisara” (11)

    • Fesito anafunsa nzeru kwa Mfumu Agiripa (13-22)

    • Paulo anaonekera kwa Agiripa (23-27)

  • 26

    • Paulo anadziteteza pamaso pa Agiripa (1-11)

    • Paulo anafotokoza mmene anakhalira Mkhristu (12-23)

    • Zimene Fesito ndi Agiripa anachita (24-32)

  • 27

    • Paulo anayenda ulendo wapanyanja wopita ku Roma (1-12)

    • Ngalawa inawonongeka ndi mphepo (13-38)

    • Ngalawa inasweka (39-44)

  • 28

    • Anafika kugombe la ku Melita (1-6)

    • Bambo ake a Papuliyo anachiritsidwa (7-10)

    • Ulendo wa ku Roma (11-16)

    • Paulo analankhula ndi Ayuda ku Roma (17-29)

    • Paulo analalikira molimba mtima kwa zaka ziwiri (30, 31)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena